Chidule cha II Mbiri I. Mbiri ya Solomo 1:1-9:31 A. Chuma chake ndi nzeru 1:1-17 B. Ntchito yake pa kachisi 2:1-7:22 C. Kutchuka kwake padziko lonse 8:1-9:31 II. Mbiri ya mafumu a Yuda 10:1–36:21 A. Kugawanika kwa ufumu 10:1-11:4 B. Kuchokera kwa Rehobowamu mpaka kwa Yehosafati 11:5-20:30 C. Kuyambira Yehoramu mpaka kugwa kwa Yerusalemu 21:1–36:21 III. Zolemba: Lamulo la Koresi 36:22-23