Chidule cha 1 Timoteo I. Mawu Oyamba 1:1-2 II. Mpingo wa Mulungu 1:3-3:16 A. Chiphunzitso chake 1:3-20 B. Kupembedza kwake 2:1-15 C. Utsogoleri wake 3:1-16 III. Utumiki wa mbusa 4:1-6:19 A. Mayendedwe ake 4:1-16 B. Ntchito yake 5:1-6:19 IV. Mawu omaliza 6:20-21