Chidule cha 1 Timoteo

I. Mawu Oyamba 1:1-2

II. Mpingo wa Mulungu 1:3-3:16
A. Chiphunzitso chake 1:3-20
B. Kupembedza kwake 2:1-15
C. Utsogoleri wake 3:1-16

III. Utumiki wa mbusa 4:1-6:19
A. Mayendedwe ake 4:1-16
B. Ntchito yake 5:1-6:19

IV. Mawu omaliza 6:20-21