Chidule cha I Mbiri 1. Mibadwo kuyambira pa Adamu mpaka pa Davide 1:1-9:44 II. Mbiri ya Mfumu Davide 10:1-29:30 A. Imfa ya Sauli 10:1-14 B. Kukwera kwa Davide pa mphamvu 11:1-12:40 C. Davide ndi likasa la chipangano 13:1–16:43 D. Zochitika mu ulamuliro wa Davide 17:1-22:1 E. Kukonzekera kwa kachisi kwa Davide 22:2-29:30